Njere yaing'ono: Nkhani ya Wangari Maathai
Peter Chamgwera
Maya Marshak
ChiChewa

M'mudzi wina wa tsinde la phiri la Kenya kum'mawa kwa Afirika, kudali mtsikana yemwe amagwila ntchito mminda ndi amaye ake.
Dzina la mtsikanayu lidali Wangari
Dzina la mtsikanayu lidali Wangari
Wangari amakonda kukhala panja.
Mmunda womwe amadzala chakudya chao anaswa mpanje
Adafesa tinjere munthakamo
Mmunda womwe amadzala chakudya chao anaswa mpanje
Adafesa tinjere munthakamo
Iye amakondetsetsa dzuwa likamalowa, pakuti madziwa kuti ndithawi yopita kunyumba.
Iye amayenda pa kanjira kakang'ono nawolokanso mitsinje pomwe amanka kunyumba
Iye amayenda pa kanjira kakang'ono nawolokanso mitsinje pomwe amanka kunyumba
Wangari adali mwana ochenjera ndipo samakhumbitsitsi kupita ku sukulu.
Atafika dzaka zisanu ndi ziwiri, mchimwene wake adakopa makolo ake kuti akayambe school
Atafika dzaka zisanu ndi ziwiri, mchimwene wake adakopa makolo ake kuti akayambe school
Iye pophunzila zambiri amazindikilanso kuti akuwakonda kwambiri anthu a ku Krnya. Iye amafuna iwo adzikhala okondwa komanso omasuka nthawi zonse
Wangari akamaphunzila amakumbukila kwao ku Afirika
Wangari akamaphunzila amakumbukila kwao ku Afirika
Atamaliza maphunzilo ake adabwelela ku Kenya.
Azimayi adalibe nkhuni zophikila chifukwa khalango yonse ija idakhala minda yolimamo mbeu zawo.
Umphawi koanso njala zidalikita anthu m'mudzimo
Azimayi adalibe nkhuni zophikila chifukwa khalango yonse ija idakhala minda yolimamo mbeu zawo.
Umphawi koanso njala zidalikita anthu m'mudzimo
Pakupita kwa nthawi; mitengoyo idakula nakhala nkhalango, ndipo izi zidathandiza kubwezeletsedwa kwa mitsinje.
Uthenga wa Wangari ufalikila dera lonse la Afirika. Lero, zikwi zikwi za mitengo idadzalidwa nakula kuchokera ku mbeu za Wangari
Uthenga wa Wangari ufalikila dera lonse la Afirika. Lero, zikwi zikwi za mitengo idadzalidwa nakula kuchokera ku mbeu za Wangari
Chifukwa cha ntchito yake yosalama za chilengedwe ndi anthu, Wangari adapaphana napeza mphoto ya maiko akunja yotchedwa Nobel Peace.
Mu chaka cha 2004, Wangari Maathai adali mzimayi wakuda kuchokera ku Afirika kupeza mphoto ya Nobel Peace komanso katswiri owona za chilengedwe
Mu chaka cha 2004, Wangari Maathai adali mzimayi wakuda kuchokera ku Afirika kupeza mphoto ya Nobel Peace komanso katswiri owona za chilengedwe
Wangari adamwalira mu chaka cha 2011, iye amakumbukilidwa nthawi zomwe pomwe taona ntengo wanthanzi.
Titha kupitiliza nthito yake podzala mitengo komanso kusamalila nkhalango zathu.
Titha kupitiliza nthito yake podzala mitengo komanso kusamalila nkhalango zathu.
You are free to download, copy, translate or adapt this story and use the illustrations as long as you attribute in the following way:
Njere yaing'ono: Nkhani ya Wangari Maathai
Author - Nicola Rijsdijk
Translation - Peter Chamgwera
Illustration - Maya Marshak
Language - ChiChewa
Level - Longer paragraphs
Translation - Peter Chamgwera
Illustration - Maya Marshak
Language - ChiChewa
Level - Longer paragraphs
© Nicola Rijsdijk, Maya Marshak, Tarryn-Anne Anderson, Bookdash.org and African Storybook Initiative 2015
Creative Commons: Attribution 4.0
Source www.africanstorybook.org
Original source www.bookdash.org
Creative Commons: Attribution 4.0
Source www.africanstorybook.org
Original source www.bookdash.org


